Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 42:29 - Buku Lopatulika

29 Ndipo anadza kwa Yakobo atate wao ku dziko la Kanani, namfotokozera iye zonse zinaonekera kwa iwo;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Ndipo anadza kwa Yakobo atate wao ku dziko la Kanani, namfotokozera iye zonse zinaonekera kwa iwo;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Atafika kwa bambo wao Yakobe, adamsimbira zonse zimene zidaŵagwera, adati,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Atafika kwa abambo awo Yakobo mʼdziko la Kanaani anafotokoza zonse zimene zinawachitikira nati,

Onani mutuwo Koperani




Genesis 42:29
5 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anati kwa abale ake, Wandibwezera ine ndalama zanga, taonani, zili kukamwa kwa thumba langa; ndipo mitima yao inawadera iwo, nanthunthumira, natembenukirana wina ndi mnzake kuti, Nchiyani ichi Mulungu watichitira ife?


kuti, Munthu mwini dziko, ananena ndi ife mwankhalwe, natiyesa ife ozonda dziko.


Ndipo panali titakwera kunka kwa kapolo wanu atate wanga, tinamfotokozera iye mau a mbuyanga.


Ndipo anakwera kutuluka mu Ejipito, nafika ku dziko la Kanani kwa Yakobo atate wao.


Ndipo anamfotokozera iye kuti, Yosefe akali ndi moyo, ndipo alamulira m'dziko lonse la Ejipito. Pamenepo mtima wake unakomoka, pakuti sanawakhulupirire iwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa