Genesis 42:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo anadza kwa Yakobo atate wao ku dziko la Kanani, namfotokozera iye zonse zinaonekera kwa iwo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo anadza kwa Yakobo atate wao ku dziko la Kanani, namfotokozera iye zonse zinaonekera kwa iwo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Atafika kwa bambo wao Yakobe, adamsimbira zonse zimene zidaŵagwera, adati, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Atafika kwa abambo awo Yakobo mʼdziko la Kanaani anafotokoza zonse zimene zinawachitikira nati, Onani mutuwo |