Genesis 42:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo iye anati kwa abale ake, Wandibwezera ine ndalama zanga, taonani, zili kukamwa kwa thumba langa; ndipo mitima yao inawadera iwo, nanthunthumira, natembenukirana wina ndi mnzake kuti, Nchiyani ichi Mulungu watichitira ife? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo iye anati kwa abale ake, Wandibwezera ine ndalama zanga, taonani, zili kukamwa kwa thumba langa; ndipo mitima yao inawadera iwo, nanthunthumira, natembenukirana wina ndi mnzake kuti, Nchiyani ichi Mulungu watichitira ife? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Adaitana abale ake naŵauza kuti, “Ha, wandibwezera ndalama zanga. Si izi zili m'thumbazi.” Pamenepo onsewo mitima yao idangoti phwii! Adachita mantha kwambiri nati, “Mulungu watichita zotani ife?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Iye anati kwa abale akewo, “Ndalama zanga andibwezera, izi zili mʼthumba mwangamu.” Mitima yawo inachita ngati yachokamo ndipo anali ndi mantha ambiri, nati, “Ndi chiyani chimene Mulungu watichitira?” Onani mutuwo |