Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 42:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo sanadziwe kuti Yosefe anamva; chifukwa anali ndi womasulira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo sanadziwe kuti Yosefe anamva; chifukwa anali ndi womasulira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Yosefe anali kumva zonse zimene ankakambiranazo, koma iwowo sadadziŵe, chifukwa choti ankalankhula naye kudzera mwa womasulira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Koma sanadziwe kuti Yosefe ankawamva popeza kuti ankagwiritsa ntchito wotanthauzira poyankhula naye.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 42:23
6 Mawu Ofanana  

Tiyeni, titsike, pomwepo tisokoneze chinenedwe chao, kuti wina asamvere chinenedwe cha mnzake.


Ndipo Rubeni anayankha nati kwa iwo, Kodi sindinanene kwa inu kuti, Musachimwire mwanayu; ndipo inu munakana kumvera? Chifukwa chakenso, taonani mwazi wake ufunidwa.


Ndipo anawafotokozera iwo nalira, nawatembenukiranso, nanena nao, nampatula Simeoni mwa iwo, nammanga iye pamaso pao.


Taonani, maso anu aona, ndi maso a mphwanga Benjamini, kuti ndi m'kamwa mwanga ndilikulankhula ndi inu.


Chifukwa chake tili atumiki m'malo mwa Khristu, monga ngati Mulungu alikudandaulira mwa ife; tiumiriza inu m'malo mwa Khristu, yanjanitsidwani ndi Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa