Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 42:20 - Buku Lopatulika

20 koma mukatenge mphwanu kudza naye kwa ine, kuti atsimikizidwe mau anu ndipo simudzafa. Ndipo anachita chomwecho.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 koma mukatenge mphwanu kudza naye kwa ine, kuti atsimikizidwe mau anu ndipo simudzafa. Ndipo anachita chomwecho.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Mng'ono wanuyo mukabwere naye kuno, kutsimikiza kuti mukunenadi zoona, ndipo simudzaphedwa.” Iwo aja adavomereza zimenezo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Mukabwere naye kuno mngʼono wanu wotsirizayo kuti titsimikizire zimene munanena kuti musafe.” Ndipo anachita zomwezo.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 42:20
12 Mawu Ofanana  

Mudzayesedwa ndi ichi, pali moyo wa Farao, simudzatuluka muno, koma akadze kuno mphwanu ndiko.


ngati muli oona, mmodzi wa abale anu amangidwe m'kaidi momwemo; mukani inu, mupite naye tirigu wa njala ya mabanja anu;


Ndipo anasenzetsa abulu ao tirigu wao nachokapo.


Ndipo munthuyo mwini dziko anati kwa ife, Momwemu ndidzadziwa kuti muli anthu oona; siyani mmodzi wa abale anu pamodzi ndi ine, tengani tirigu wa njala ya kwanu, mukani;


idzani naye mphwanu kwa ine, ndipo ndidzadziwa kuti simuli ozonda koma anthu oona: chomwecho ndidzakubwezerani inu mbale wanu, ndipo mudzachita malonda m'dziko muno.


Ndipo anayandikira kwa tsanyumba wa Yosefe, ndipo ananena ndi iye pa khomo la nyumba, nati,


Ndipo Yuda ananena ndi iye kuti, Munthu uja anatilimbitsira mau kuti, simudzaonanso nkhope yanga, koma mphwanu akhale ndi inu ndiko.


Koma mukapanda kumtuma iye sititsika; pakuti munthu uja anati kwa ife, Simudzaona nkhope yanga, ngati mphwanu sali ndi inu.


Ndipo munati kwa akapolo anu, Munditengere iye, kuti ndimuone iye m'maso mwanga.


Ndipo munati kwa akapolo anu, Koma ngati mbale wanu safika pamodzi ndi inu, simudzaonanso konse nkhope yanga.


Chotero anachita Nowa, monga mwa zonse anamlamulira iye Mulungu, momwemo anachita.


Amake ananena kwa atumiki, Chimene chilichonse akanena kwa inu, chitani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa