Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 42:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo iye anati kwa iwo, Iai, koma mwadzera kuti muone usiwa wa dziko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo iye anati kwa iwo, Iai, koma mwadzera kuti muone usiwa wa dziko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Yosefe adati, “Iyai. Inu mwabwera kudzazonda dziko lathu kuti muwone ngati ndi lofooka.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Iye anawawuza kuti, “Ayi! Inu mwabwera kudzaona pamene palibe chitetezo mʼdziko muno.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 42:12
4 Mawu Ofanana  

Tonse tili ana aamuna a munthu mmodzi; tili oona, akapolo anu, sitili ozonda.


Nati iwo, Akapolo anu ndife abale khumi, ana aamuna a munthu mmodzi m'dziko la Kanani; ndipo, taonani, wamng'ono ali ndi atate wathu lero; ndipo palibe mmodzi.


Mudzayesedwa ndi ichi, pali moyo wa Farao, simudzatuluka muno, koma akadze kuno mphwanu ndiko.


Mumdziwa Abinere mwana wa Nere kuti anadza kuti akunyengeni, ndi kuti adziwe kutuluka kwanu ndi kulowa kwanu, ndi kuti adziwe zonse mulikuchita inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa