Genesis 41:52 - Buku Lopatulika52 Ndipo dzina la wachiwiri anamutcha Efuremu: chifukwa Mulungu anandibalitsa ine m'dziko la kusauka kwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201452 Ndipo dzina la wachiwiri anamutcha Efuremu: chifukwa Mulungu anandibalitsa ine m'dziko la kusauka kwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa52 Ndipo adanenanso kuti, “Mulungu wandipatsa ana m'dziko la masautso anga.” Motero mwana wachiŵiriyo adamutcha Efuremu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero52 Mwana wachiwiri wa mwamuna anamutcha Efereimu popeza anati, “Mulungu wandipatsa ana mʼdziko la masautso anga.” Onani mutuwo |