Genesis 41:51 - Buku Lopatulika51 Ndipo Yosefe anamutcha dzina la woyamba Manase, chifukwa anati iye, Mulungu wandiiwalitsa ine zovuta zanga zonse, ndi nyumba yonse ya atate wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201451 Ndipo Yosefe anamutcha dzina la woyamba Manase, chifukwa anati iye, Mulungu wandiiwalitsa ine zovuta zanga zonse, ndi nyumba yonse ya atate wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa51 Tsono adati, “Mulungu wandiiŵalitsa kusauka kwanga konse kuja ndiponso banja la atate anga.” Motero mwana wake wachisamba uja adamutcha Manase. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero51 Yosefe anamutcha mwana wake woyamba, Manase popeza anati, “Mulungu wandiyiwalitsa zovuta zanga zija ndiponso banja la abambo anga.” Onani mutuwo |