Genesis 41:31 - Buku Lopatulika31 ndipo zochuluka sizidzazindikirika chifukwa cha njala ikudza m'mbuyoyo, pakuti idzavuta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 ndipo zochuluka sizidzazindikirika chifukwa cha njala ikudza m'mbuyoyo, pakuti idzavuta. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Zaka zonse zija za dzinthu dzambiri sizidzakumbukikanso, chifukwa njala imene idzabwereyo idzakhala yoopsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Zakudya zochuluka za mʼdzikomo zija sizidzakumbukirikanso chifukwa njala imene iti idzabwereyo idzakhala yoopsa. Onani mutuwo |