Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 41:28 - Buku Lopatulika

28 Ichi ndi chinthu chimene ndinena kwa Farao: chimene Mulungu ati achite wasonyeza kwa Farao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Ichi ndi chinthu chimene ndinena kwa Farao: chimene Mulungu ati achite wasonyeza kwa Farao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Tsono monga momwe ndanenera, ndiye kuti Mulungu wakuuziranitu zomwe adzachite.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 “Tsono ndi monga ndafotokozeramu kuti Mulungu wakuwuziranitu zimene adzachite.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 41:28
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yosefe anati kwa iye, Kumasulira kwake ndi uwu: nthambi zitatu ndizo masiku atatu;


Ndipo Yosefe anayankha Farao kuti, Si mwa ine; koma Mulungu adzayankha Farao mwamtendere.


Ndipo Yosefe anati kwa Farao, Loto la Farao lili limodzi: chimene Mulungu ati achite wam'masulira Farao.


Ndipo lotolo linabwerezedwa kawiri kwa Farao, chifukwa chinthu chili chokhazikika ndi Mulungu, ndipo Mulungu afulumira kuchichita.


Umo mudaonera kuti mwala unasemedwa m'phiri popanda manja, ndi kuti udapera chitsulo, mkuwa, dongo, siliva, ndi golide; Mulungu wamkulu wadziwitsa mfumu chidzachitika m'tsogolomo; lotoli nloona, ndi kumasulira kwake kwakhazikika.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa