Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 41:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo Farao ananena kwa Yosefe, M'loto langa taona, ndinaima m'mphepete mwa mtsinje;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo Farao ananena kwa Yosefe, M'loto langa taona, ndinaima m'mphepete mwa nyanja;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Apo Farao adati, “Ine ndidaalota ntaimirira pamphepete pa mtsinje wa Nailo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Ndipo Farao anati kwa Yosefe, “Ndinalota nditayimirira mʼmphepete mwa mtsinje wa Nailo,

Onani mutuwo Koperani




Genesis 41:17
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Yosefe anayankha Farao kuti, Si mwa ine; koma Mulungu adzayankha Farao mwamtendere.


ndipo taona, zinatuluka m'mtsinjemo ng'ombe zazikazi zisanu ndi ziwiri, zonenepa ndi za maonekedwe abwino; ndipo zinadya m'mabango;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa