Genesis 41:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo Yosefe anayankha Farao kuti, Si mwa ine; koma Mulungu adzayankha Farao mwamtendere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo Yosefe anayankha Farao kuti, Si mwa ine; koma Mulungu adzayankha Farao mwamtendere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Yosefe adayankha kuti, “Sindine ai, koma Mulungu ndiye amene adzatha kuimasulira mfumu maloto ameneŵa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Yosefe anamuyankha Farao kuti, “Sindingathe koma Mulungu apereka yankho limene Farao akufuna.” Onani mutuwo |