Genesis 41:15 - Buku Lopatulika15 Farao ndipo anati kwa Yosefe, Ine ndalota loto, koma palibe wondimasulira; ndipo ndamva alikunena za iwe kuti, ukamva loto udziwa kumasulira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Farao ndipo anati kwa Yosefe, Ine ndalota loto, koma palibe wondimasulira; ndipo ndamva alikunena za iwe kuti, ukamva loto udziwa kumasulira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Farao adauza Yosefe kuti, “Ine ndidalota maloto, koma palibe ndi mmodzi yemwe amene akutha kumasula malotowo. Tsono adandiwuza kuti iwe ukamva maloto, ati umadziŵa kumasula kwake.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Farao anati kwa Yosefe, “Ndinalota maloto ndipo palibe amene watha kunditanthauzira. Tsono ndawuzidwa kuti iwe ukamva loto umadziwanso kulimasulira.” Onani mutuwo |