Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 40:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo Yosefe analowa kwa iwo m'mawa, nawaona iwo, taonani, anali oziya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo Yosefe analowa kwa iwo m'mawa, nawaona iwo, taonani, anali oziya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Yosefe atabwera m'maŵa, adaona kuti nkhope zao zasinthika.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Mmawa wake, Yosefe atabwera, anaona kuti nkhope zawo zinali zakugwa.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 40:6
9 Mawu Ofanana  

Ndipo analota maloto onse awiri, yense loto lake, usiku umodzi, yense monga mwa kumasulira kwa loto lake, wopereka chikho ndi wophika mkate wa mfumu ya Aejipito, amene anamangidwa m'kaidi.


Ndipo anafunsa akulu a Farao osungidwa naye m'nyumba ya mbuyake, kuti, Nkhope zanu zagwa bwanji lero?


Ndipo iwo anati kwa iye, Ife talota maloto, ndipo tilibe wotimasulira. Ndipo Yosefe anati kwa iwo, Kodi Mwini kumasulira si ndiye Mulungu? Mundifotokozeretu.


Ndipo panali m'mamawa mtima wake unavutidwa; ndipo anatumiza naitana amatsenga onse a mu Ejipito, ndi anzeru onse a momwemo: ndipo Farao anafotokozera iwo loto lake; koma panalibe mmodzi anakhoza kuwamasulira iwo kwa Farao.


Ndinaona loto lakundiopsa, ndi zolingirira za pakama panga, ndi masomphenya a m'mtima mwanga, zinandivuta ine.


Pamenepo padasandulika pa nkhope pake pa mfumu, ndi maganizo ake anamsautsa, ndi mfundo za m'chuuno mwake zinaguluka, ndi maondo ake anaombana.


Kutha kwake kwa chinthuchi nkuno. Ine Daniele, maganizo anga anandivuta kwambiri, ndi nkhope yanga inasandulika; koma ndinasunga chinthuchi m'mtima mwanga.


Ndipo ine Daniele ndinakomoka ndi kudwala masiku ena; pamenepo ndinauka ndi kuchita ntchito ya mfumu; ndipo ndinadabwa nao masomphenyawo, koma panalibe wakuwazindikiritsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa