Genesis 40:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo Yosefe analowa kwa iwo m'mawa, nawaona iwo, taonani, anali oziya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo Yosefe analowa kwa iwo m'mawa, nawaona iwo, taonani, anali oziya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Yosefe atabwera m'maŵa, adaona kuti nkhope zao zasinthika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mmawa wake, Yosefe atabwera, anaona kuti nkhope zawo zinali zakugwa. Onani mutuwo |