Genesis 40:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo anafunsa akulu a Farao osungidwa naye m'nyumba ya mbuyake, kuti, Nkhope zanu zagwa bwanji lero? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo anafunsa akulu a Farao osungidwa naye m'nyumba ya mbuyake, kuti, Nkhope zanu zagwa bwanji lero? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Adaŵafunsa kuti, “Mwatani mukuwoneka ngati achisoni lero?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Choncho anafunsa akuluakulu a kwa Farao amene anali naye mʼndende muja kuti, “Bwanji nkhope zanu zili zachisoni lero?” Onani mutuwo |