Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 40:23 - Buku Lopatulika

23 Koma wopereka chikho wamkulu sanakumbukire Yosefe, koma anamuiwala.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Koma wopereka chikho wamkulu sanakumbukire Yosefe, koma anamuiwala.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Komabe woperekera vinyo uja sadamkumbuke Yosefe, adangomuiŵaliratu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Koma mkulu wa operekera zakumwa uja sanamukumbukire Yosefe ndipo anamuyiwaliratu.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 40:23
9 Mawu Ofanana  

Ndipo panali zitapita zaka ziwiri zamphumphu, Farao analota; ndipo, taonani, anaima pamtsinje.


Pamenepo wopereka chikho wamkulu anati kwa Farao, kuti, Ine ndidzakumbukira zochimwa zanga lero.


Niti mfumu, Anamchitira Mordekai ulemu ndi ukulu wotani chifukwa cha ichi? Ndipo anyamata a mfumu akuitumikira ananena nayo, Sanamchitire kanthu.


Anansi anga andisowa, ndi odziwana nane bwino andiiwala.


kufikira nyengo yakuchitika maneno ake; mau a Yehova anamuyesa.


Ndaiwalika m'mtima monga wakufa, ndikhala monga chotengera chosweka.


Pakuti ndamva ugogodi wa ambiri, mantha andizinga. Pondipangira chiwembu, anatsimikiza mtima kulanda moyo wanga.


akumwera vinyo m'zipanda, nadzidzoza ndi mafuta abwino oposa, osagwidwa chisoni ndi kuthyoka kwa Yosefe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa