Genesis 40:19 - Buku Lopatulika19 akali masiku atatu Farao adzakweza mutu wako ndi kuuchotsa, nadzakupachika iwe pamtengo: ndipo mbalame zidzadya mnofu wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 akali masiku atatu Farao adzakweza mutu wako ndi kuuchotsa, nadzakupachika iwe pamtengo: ndipo mbalame zidzadya mnofu wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Pakapita masiku atatu, Farao akutulutsa muno, ndipo adzadula mutu wako. Tsono mtembo wako adzaupachika pa mtengo, ndipo mbalame zidzadya mnofu wako.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Pakangotha masiku atatu Farao adzakutulutsa muno koma adzakupachika. Ndipo mbalame zidzadya mnofu wako.” Onani mutuwo |