Genesis 40:10 - Buku Lopatulika10 ndipo m'mpesamo munali nthambi zitatu: ndipo unali wonga unaphuka, ndipo maluwa ake anaphuka; nabala matsamvu ake mphesa zakucha; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 ndipo m'mpesamo munali nthambi zitatu: ndipo unali wonga unaphuka, ndipo maluwa ake anaphuka; nabala matsamvu ake mphesa zakucha; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 unali ndi nthambi zitatu. Masamba ake atangophukira, pomwepo panaoneka maluŵa, pambuyo pake panaonekanso mphesa zakupsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 unali ndi nthambi zitatu. Mpesawo utangophukira, unachita maluwa ndipo maphava ake anabereka mphesa zakupsa. Onani mutuwo |