Genesis 4:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo panali atapita masiku, Kaini anatenga zipatso za nthaka, nsembe ya kwa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo panali atapita masiku, Kaini anatenga zipatso za nthaka, nsembe ya kwa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Patapita nthaŵi, Kaini adatenga zipatso zina zakumunda, nazipereka kwa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Patapita nthawi, Kaini anatenga zipatso za ku munda nakazipereka kwa Yehova monga nsembe. Onani mutuwo |