Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 4:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Patapita nthawi, Kaini anatenga zipatso za ku munda nakazipereka kwa Yehova monga nsembe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

3 Ndipo panali atapita masiku, Kaini anatenga zipatso za nthaka, nsembe ya kwa Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo panali atapita masiku, Kaini anatenga zipatso za nthaka, nsembe ya kwa Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Patapita nthaŵi, Kaini adatenga zipatso zina zakumunda, nazipereka kwa Chauta.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 4:3
7 Mawu Ofanana  

Kenaka anabereka mʼbale wake Abele. Abele anali woweta nkhosa ndipo Kaini anali mlimi.


Nayenso Abele anatenga ana ankhosa oyamba kubadwa pamodzi ndi mafuta ake nakazipereka ngati nsembe kwa Yehova. Yehova anakondwera ndi Abele ndi nsembe yake.


Patapita masiku, mtsinjewo unaphwa chifukwa mvula sinagwe mʼdzikomo.


Koma pamene izi zonse zinkachitika mu Yerusalemu, ine kunalibe popeza mʼchaka cha 32 cha Aritasasita mfumu ya Babuloni ine ndinabwerera kwa mfumu. Patapitanso nthawi ndinapempha chilolezo kwa mfumuyo


“Ndikukupatsani mafuta onse abwino kwambiri a olivi ndi vinyo yense watsopano wabwino kwambiri ndi tirigu yense zomwe Aisraeli amapereka kwa Yehova ngati zipatso zoyamba pa zokolola zawo.


Tsoka kwa iwo chifukwa anatsatira njira ya Kaini. Iwo athamangira phindu, nʼchifukwa chake anagwa mʼtchimo la Baalamu. Iwo anawonongedwa chifukwa chowukira monga anachitira Kora.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa