Genesis 4:11 - Buku Lopatulika11 Tsopano ndiwe wotembereredwa kunthaka, imene inatsegula pakamwa pake kulandira padzanja lako mwazi wa mphwako: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Tsopano ndiwe wotembereredwa kunthaka, imene inatsegula pakamwa pake kulandira pa dzanja lako mwazi wa mphwako: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsopano watembereredwa, sudzailimanso nthaka yomwe yamwa magazi a mng'ono wako, amene waŵakhetsa ndi manja ako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ndipo tsopano ndiwe wotembereredwa ndipo wachotsedwa mʼdziko limene nthaka yake inatsekula pakamwa pake kulandira magazi a mʼbale wako amene unakhetsa. Onani mutuwo |