Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 39:18 - Buku Lopatulika

18 ndipo panali pamene ndinakweza mau anga ndi kufuula, iye anasiya chovala chake kwa ine, nathawira kunja.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 ndipo panali pamene ndinakweza mau anga ndi kufuula, iye anasiya chovala chake kwa ine, nathawira kunja.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Koma ine nditakuwa, iyeyo anasiya mwinjiro wake pafupi ndi ine, nkuthaŵira pabwalo.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Koma pamene ndinakuwa, iye anandisiyira mkanjo wake nathawira kunja.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 39:18
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ananena kwa iye monga mau awa, anati, Analowa kwa ine kapolo wa Chihebri uja, munabwera naye kwathu, kundipunza ine:


Ndipo panali pamene mbuyake anamva mau a mkazi wake, amene ananena kwa iye, kuti, Choterochi anandichitira ine kapolo wako; kuti iye anapsa mtima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa