Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 38:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo Yuda anati kwa Onani, Lowani naye mkazi wa mbale wako, ndi kumchitira mkazi zoyenera mphwake wa mwamuna wake, ndi kumuukitsira mkulu wako mbeu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo Yuda anati kwa Onani, Lowani naye mkazi wa mbale wako, ndi kumchitira mkazi zoyenera mphwake wa mwamuna wake, ndi kumuukitsira mkulu wako mbeu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Motero Yuda adauza Onani kuti, “Loŵana naye mkazi wamasiye wa mbale wakoyu. Uloŵe chokolo ndithu, kuti mbale wakoyo akhale ndi ana.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Pamenepo Yuda anati kwa Onani, “Kwatira mkazi wamasiye wa mʼbale wako. Ulowe chokolo kuti mʼbale wako akhale ndi mwana.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 38:8
7 Mawu Ofanana  

Woyamba ndipo anati kwa wamng'ono, Atate wathu akalamba, ndipo palibe padziko lapansi mwamuna amene adzalowa kwa ife monga amachita padziko lonse lapansi:


Usamavula mkazi wa mbale wako; ndiye thupi la mbale wako.


Nati Naomi, Bwererani, ana anga, mudzatsagana nane bwanji? Ngati ndili nao m'mimba mwanga ana aamuna ena kuti akhale amuna anu?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa