Genesis 38:7 - Buku Lopatulika7 Koma Eri mwana wake woyamba wa Yuda anali woipa pamaso pa Yehova: ndipo Yehova anamupha iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Koma Eri mwana wake woyamba wa Yuda anali woipa pamaso pa Yehova: ndipo Yehova anamupha iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Koma makhalidwe oipa a Ere adaipira Chauta, mwakuti Chauta adamlanga ndi imfa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Koma ntchito zoyipa za Eri, mwana wachisamba wa Yuda zinayipira Yehova. Choncho Mulungu anamulanga ndi imfa. Onani mutuwo |