Genesis 37:34 - Buku Lopatulika34 Yakobo ndipo anang'amba malaya ake, na vala chiguduli m'chuuno mwake namlirira mwana wake masiku ambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Yakobo ndipo anang'amba malaya ake, navala chiguduli m'chuuno mwake namlirira mwana wake masiku ambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Yakobe adang'amba zovala zake, navala chiguduli m'chiwuno, chifukwa cha chisoni. Adalira maliro a mwana wakeyo nthaŵi yaitali. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Pamenepo Yakobo anangʼamba zovala zake, navala chisaka mʼchiwuno mwake. Iye analira maliro a mwana wake masiku ambiri. Onani mutuwo |