Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 37:32 - Buku Lopatulika

32 natumiza malaya amwinjiro, nadza nao kwa atate ao: ndipo anati, Siwa tawatola; muzindikire tsono ngati ndi malaya a mwana wanu, kapena ndi ena.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 natumiza malaya amwinjiro, nadza nao kwa atate ao: ndipo anati, Siwa tawatola; muzindikire tsono ngati ndi malaya a mwana wanu, kapena ndi ena.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Adatenga mkanjowo napita nawo kwa bambo wao, nati, “Tayang'anani, kapena nkukhala mkanjo wa mwana wanu uja.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Iwo anatenga mkanjo uja nabwerera nawo kwa abambo awo nati, “Ife tapeza mkanjowu. Tawuyangʼanitsitsani muone ngati uli wa mwana wanu.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 37:32
7 Mawu Ofanana  

Tiyeni tsopano timuphe iye timponye m'dzenje, ndipo tidzati, Wajiwa ndi chilombo; ndipo tidzaona momwe adzachita maloto ake.


Koma Israele anamkonda Yosefe koposa ana ake onse, pakuti anali mwana wa ukalamba wake; ndipo anamsokera iye malaya amwinjiro.


Ndipo anatenga malaya ake a Yosefe, napha tonde, naviika malaya m'mwazi wake:


Ndipo anazindikira nati, Ndiwo malaya a mwana wanga: wajiwa ndi chilombo: Yosefe wakadzulidwa ndithu.


Pamene anamtulutsa iye, mkazi anatumiza kwa mpongozi wake kuti, Ndi mwamuna mwini izi ndatenga pakati; ndipo mkazi anati, Tayang'anatu, za yani zimenezi, mphete, ndi chingwe, ndi ndodo?


Koma pamene anadza mwana wanu uyu, wakutha zamoyo zanu ndi akazi achiwerewere, munamphera iye mwanawang'ombe wonenepa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa