Genesis 37:31 - Buku Lopatulika31 Ndipo anatenga malaya ake a Yosefe, napha tonde, naviika malaya m'mwazi wake: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ndipo anatenga malaya ake a Yosefe, napha tonde, naviika malaya m'mwazi wake: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Pomwepo iwo adapha mbuzi, naviika mkanjo wa Yosefe uja m'magazi ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Tsono anapha kamwana ka mbuzi, natenga mkanjo wa Yosefe ndi kuwunyika mʼmagazi ake. Onani mutuwo |