Genesis 37:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo panali pamene Yosefe anafika kwa abale ake, anamvula Yosefe malaya ake, malaya amwinjiro amene anavala iye; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo panali pamene Yosefe anafika kwa abale ake, anamvula Yosefe malaya ake, malaya amwinjiro amene anavala iye; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Yosefe atafika kumene kunali abale akewo, iwowo adamuvula mkanjo wake, uja wautali wamanjawu umene adaavala, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Choncho Yosefe atafika kwa abale ake, iwo anamuvula mkanjo wake wamanja aatali uja umene anavala Onani mutuwo |