Genesis 37:24 - Buku Lopatulika24 ndipo anamtenga iye, namponya m'dzenjemo; m'dzenjemo munalibe kanthu, munalibe madzi m'menemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 ndipo anamtenga iye, namponya m'dzenjemo; m'dzenjemo munalibe kanthu, munalibe madzi m'menemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 namtenga, nkumuponya m'chitsime chopanda madzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 ndipo anamutenga namuponya mʼchitsime chopanda madzi komanso mopanda chilichonse. Onani mutuwo |