Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 37:21 - Buku Lopatulika

21 Ndipo Rubeni anamva nampulumutsa iye m'manja mwao; nati, Tisamuphe iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Ndipo Rubeni anamva nampulumutsa iye m'manja mwao; nati, Tisamuphe iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Tsono Rubeni adamva zimene enawo ankanena, ndipo adayesetsa kumpulumutsa Yosefe. Adati, “Ai tisamuphe, tisakhetse magazi ake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Koma Rubeni atamva izi, anapulumutsa Yosefe. Iye anati kwa abale ake, “Ayi, tisamuphe,

Onani mutuwo Koperani




Genesis 37:21
6 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene Israele anakhala m'dzikomo, Rubeni anamuka nagona ndi Biliha, mkazi wamng'ono wa atate wake: ndipo Israele anamva. Ana aamuna a Yakobo anali khumi ndi awiri:


Ndipo Rubeni anati kwa iwo, Musakhetse mwazi; mponyeni iye m'dzenjemo m'chipululu muno, koma musamsamulire iye manja: kuti ampulumutse iye m'manja mwao, ambwezenso kwa atate wake.


Ndipo Rubeni anayankha nati kwa iwo, Kodi sindinanene kwa inu kuti, Musachimwire mwanayu; ndipo inu munakana kumvera? Chifukwa chakenso, taonani mwazi wake ufunidwa.


Zoonatu mwazi wanu wa miyoyo yanu ndidzafuna; padzanja la zinyama zonse ndidzaufuna: ndi padzanja la munthu, padzanja la mbale wake wa munthu ndidzaufuna moyo wa munthu.


Ndipo musamaopa amene akupha thupi, koma moyo sangathe kuupha; koma makamaka muope Iye, wokhoza kuononga moyo ndi thupi lomwe muGehena.


Ndipo Yoswa anagwira Makeda tsiku lomwe lija ndi kuukantha ndi lupanga lakuthwa, ndi mfumu yake yomwe; anawaononga konse, ndi amoyo onse anali m'mwemo, osasiyapo ndi mmodzi yense, nachitira mfumu ya ku Makeda monga anachitira mfumu ya ku Yeriko.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa