Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 37:19 - Buku Lopatulika

19 Ndipo anati wina ndi mnzake, Taonani, alinkudza mwini maloto uja.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndipo anati wina ndi mnzake, Taonani, alinkudza mwini maloto uja.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Onsewo ankauzana kuti, “Uyotu kamaloto uja, akudza apoyo!

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Iwo anawuzana nati, “Uyo akubwera apo wamaloto uja.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 37:19
6 Mawu Ofanana  

Ndipo analota, taonani, makwerero anaima pansi, pamwamba pake ndipo padafikira kumwamba: ndipo, taonani, amithenga a Mulungu analinkukwera, analinkutsika pamenepo.


Ndipo abale ake anamchitira iye nsanje, koma atate wake anasunga mau amene m'mtima mwake.


Ndipo iwo anamuona iye ali patali, ndipo asanayandikire pafupi ndi iwo, anampangira iye chiwembu kuti amuphe.


Tiyeni tsopano timuphe iye timponye m'dzenje, ndipo tidzati, Wajiwa ndi chilombo; ndipo tidzaona momwe adzachita maloto ake.


Yosefe ndipo analota loto, nawafotokozera abale ake; ndipo anamuda iye koposa.


Eni uta anavutitsa iye kwambiri, namponyera iye, namzunza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa