Genesis 37:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo anati wina ndi mnzake, Taonani, alinkudza mwini maloto uja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo anati wina ndi mnzake, Taonani, alinkudza mwini maloto uja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Onsewo ankauzana kuti, “Uyotu kamaloto uja, akudza apoyo! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Iwo anawuzana nati, “Uyo akubwera apo wamaloto uja. Onani mutuwo |