Genesis 37:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo iwo anamuona iye ali patali, ndipo asanayandikire pafupi ndi iwo, anampangira iye chiwembu kuti amuphe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo iwo anamuona iye ali patali, ndipo asanayandikire pafupi ndi iwo, anampangira iye chiwembu kuti amuphe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Abale ake aja adamuwonera kutali, iye asanayandikire nkomwe pamene panali iwopo. Adayamba kumpangira chiwembu natsimikiza zoti amuphe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Abale ake aja anamuonera patali. Ndipo asanafike nʼkomwe kumene kunali iwo kuja, anayamba kale kumupangira chiwembu choti amuphe. Onani mutuwo |