Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 37:17 - Buku Lopatulika

17 Munthuyo ndipo anati, Anachoka pano; pakuti ndinamva alinkuti, Timuke ku Dotani. Yosefe ndipo anatsata abale ake, nawapeza ali ku Dotani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Munthuyo ndipo anati, Anachoka pano; pakuti ndinamva alinkuti, Timuke ku Dotani. Yosefe ndipo anatsata abale ake, nawapeza ali ku Dotani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Munthuyo adati, “Adachoka kale kuno. Ndidaŵamva akunena kuti akupita ku Dotani.” Apo Yosefe adaŵalondola abale akewo, nakaŵapeza ku Dotani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Munthuyo anayankha nati, “Anasamukako kuno. Ndinawamva akuti, ‘Tiyeni tipite ku Dotani.’ ” Choncho Yosefe analondola abale ake ndipo anakawapeza ku Dotani.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 37:17
2 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anati, Ndifuna abale anga. Undiuzetu kumene adyetsa zoweta.


Nati iye, Kamuoneni komwe ali; ndikatume munthu kumtenga. Ndipo anamuuza kuti, Ali ku Dotani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa