Genesis 37:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo iye anati, Ndifuna abale anga. Undiuzetu kumene adyetsa zoweta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo iye anati, Ndifuna abale anga. Undiuzetu kumene adyetsa zoweta. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 “Ndikufunafuna abale anga. Chonde tandiwuzani kumene akuŵeta nkhosa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Iye anayankha, “Ndikufuna abale anga. Mungandiwuze kumene akudyetsa ziweto zawo?” Onani mutuwo |