Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 37:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo iye anati, Ndifuna abale anga. Undiuzetu kumene adyetsa zoweta.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo iye anati, Ndifuna abale anga. Undiuzetu kumene adyetsa zoweta.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 “Ndikufunafuna abale anga. Chonde tandiwuzani kumene akuŵeta nkhosa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Iye anayankha, “Ndikufuna abale anga. Mungandiwuze kumene akudyetsa ziweto zawo?”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 37:16
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anampeza munthu, taonani, analinkusokera m'thengo; munthuyo ndipo anamfunsa, nati, Kodi ufuna chiyani?


Munthuyo ndipo anati, Anachoka pano; pakuti ndinamva alinkuti, Timuke ku Dotani. Yosefe ndipo anatsata abale ake, nawapeza ali ku Dotani.


Ndiuze, iwe amene moyo wanga ukukonda, umaweta kuti gulu lako? Umaligonetsa kuti pakati pa usana? Pakuti ndikhalirenji ngati wosochera pambali pa magulu a anzako?


Pakuti Mwana wa Munthu anadza kufunafuna ndi kupulumutsa chotayikacho.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa