Genesis 37:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo anampeza munthu, taonani, analinkusokera m'thengo; munthuyo ndipo anamfunsa, nati, Kodi ufuna chiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo anampeza munthu, taonani, analinkusokera m'thengo; munthuyo ndipo anamfunsa, nati, Kodi ufuna chiyani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 munthu wina adampeza akungoyendayenda m'deralo namufunsa kuti, “Kodi ukufunafuna chiyani?” Yosefe adayankha kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 munthu wina anamupeza akungozungulirazungulira mʼmunda ndipo anamufunsa, “Ukufunafuna chiyani?” Onani mutuwo |