Genesis 37:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo abale ake ananka kukaweta zoweta za atate wao mu Sekemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo abale ake ananka kukaweta zoweta za atate wao m'Sekemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Tsiku lina abale ake a Yosefe adapita ku Sekemu kukaŵeta nkhosa za bambo wao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Tsono abale ake anapita kukadyetsa ziweto za abambo awo ku Sekemu, Onani mutuwo |