Genesis 37:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo abale ake anamchitira iye nsanje, koma atate wake anasunga mau amene m'mtima mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo abale ake anamchitira iye nsanje, koma atate wake anasunga mau amene m'mtima mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono abale ake aja adachita naye kaduka kwambiri. Koma atate ake ankakhala akuziganiza zimenezi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Abale ake anamuchitira nsanje, koma abambo ake anasunga nkhaniyi mu mtima. Onani mutuwo |