Genesis 37:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo iye anafotokozera atate wake ndi abale ake; ndipo atate wake anamdzudzula, nati kwa iye, Loto limene walota iwe nlotani? Kodi ine ndi amai ako ndi abale ako tidzafika ndithu tokha kuweramira iwe pansi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo iye anafotokozera atate wake ndi abale ake; ndipo atate wake anamdzudzula, nati kwa iye, Loto limene walota iwe nlotani? Kodi ine ndi amai ako ndi abale ako tidzafika ndithu tokha kuweramira iwe pansi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Maloto ameneŵa adauzanso bambo wake pamodzi ndi abale ake omwe aja. Atate ake adamdzudzula, adati, “Kodi maloto ameneŵa ngotani? Kodi ukuganiza kuti ine, mai wakoyu pamodzi ndi abale akoŵa, tidzakugwadira iwe?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Atawuza abambo ake ndi abale ake malotowa, abambo ake anamukalipira nati, “Ndi maloto anji umalotawa? Kodi uganiza kuti ine, amayi ako pamodzi ndi abale ako onsewa tingadzabwere kudzakugwandira iwe?” Onani mutuwo |