Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 34:23 - Buku Lopatulika

23 Kodi ng'ombe zao ndi chuma chao ndi zoweta zao sizidzakhala zathu? Pokhapo tivomerezana nao ndipo adzakhala pamodzi ndi ife.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Kodi ng'ombe zao ndi chuma chao ndi zoweta zao sizidzakhala zathu? Pokhapo tivomerezana nao ndipo adzakhala pamodzi ndi ife.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Nanga sindiye kuti zoŵeta zao, katundu wao ndi ng'ombe zao zidzakhala zathu? Motero tiyeni tivomere kuti azikhala pakati pathu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Tikatero, ndiye kuti ziweto zawo zonsezi, katundu wawo yenseyu ndi ziweto zawo zina zonsezi zidzakhala zathu. Choncho tiyeni tiwavomereze ndipo adzakhazikika pakati pathu.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 34:23
9 Mawu Ofanana  

Anthuwo adzatiloleza ife tikhale nao anthu amodzi, pokhapo amuna onse a mwa ife adzadulidwa, monga iwo adulidwa.


Ndipo onse amene anatuluka pa chipata cha mzinda wao anamvera Hamori ndi mwana wake Sekemu, nadulidwa amuna onse akutuluka pa chipata cha mzinda wao.


Munthu wokhulupirika ali ndi madalitso ambiri; koma wokangaza kulemera sadzapulumuka chilango.


nati kwa iwo akugulitsa nkhunda, Chotsani izi muno; musamayesa nyumba ya Atate wanga nyumba ya malonda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa