Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 34:18 - Buku Lopatulika

18 Mau ao ndipo anakomera Hamori ndi Sekemu mwana wake wa Hamori.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Mau ao ndipo anakomera Hamori ndi Sekemu mwana wake wa Hamori.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Mau ameneŵa adakondweretsa kwambiri Hamori ndi mwana wake Sekemu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Mawu amenewa anakondweretsa Hamori ndi mwana wake Sekemu.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 34:18
3 Mawu Ofanana  

Koma mukapanda kutimvera ndi kusadulidwa, pamenepo tidzatenga mwana wathu wamkazi, ndi kumuka naye.


Ndipo mnyamatayo sanachedwe kuchichita popeza anakondwera ndi mwana wake wamkazi wa Yakobo; ndipo iye anali wolemekezedwa woposa onse a pa banja la atate wake.


Ndipo mbiri yake inamveka m'nyumba ya Farao, kuti abale ake a Yosefe afika; ndipo inamkomera Farao, ndi anyamata ake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa