Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 34:17 - Buku Lopatulika

17 Koma mukapanda kutimvera ndi kusadulidwa, pamenepo tidzatenga mwana wathu wamkazi, ndi kumuka naye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Koma mukapanda kutimvera ndi kusadulidwa, pamenepo tidzatenga mwana wathu wamkazi, ndi kumuka naye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Koma ngati simuvomereza zimene tikunenazi, zoti muumbalidwe, ife tidzangomtenga mwana wathu wamkaziyu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Koma ngati simuvomereza kuchita mdulidwe titenga mlongo wathu ndi kupita.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 34:17
2 Mawu Ofanana  

pamenepo tidzakupatsani inu ana athu aakazi, ndipo tidzadzitengera ana anu aakazi, ndipo tidzakhala pamodzi ndi inu, ndi kukhala mtundu umodzi.


Mau ao ndipo anakomera Hamori ndi Sekemu mwana wake wa Hamori.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa