Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 34:16 - Buku Lopatulika

16 pamenepo tidzakupatsani inu ana athu aakazi, ndipo tidzadzitengera ana anu aakazi, ndipo tidzakhala pamodzi ndi inu, ndi kukhala mtundu umodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 pamenepo tidzakupatsani inu ana athu akazi, ndipo tidzadzitengera ana anu akazi, ndipo tidzakhala pamodzi ndi inu, ndi kukhala mtundu umodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Pamenepo tidzakulolani kuti mukwatire ana athu, ndipo ifenso tidzakwatira ana anu. Tsono tidzakhazikika pakati panu ndi kusanduka fuko limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Kenaka tidzakulolani kuti mukwatire ana athu, ifenso tizikwatira ana anu. Choncho tidzakhala pakati panu ndipo tidzakhala anthu amodzi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 34:16
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Isaki anamuitana Yakobo, namdalitsa iye, namuuza iye, nati kwa iye, Usatenge mkazi wa ana aakazi a Kanani.


Koma apa pokha tidzakuvomerezani: ngati mudzakhala onga ife ndi kudulidwa amuna onse;


Koma mukapanda kutimvera ndi kusadulidwa, pamenepo tidzatenga mwana wathu wamkazi, ndi kumuka naye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa