Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 34:15 - Buku Lopatulika

15 Koma apa pokha tidzakuvomerezani: ngati mudzakhala onga ife ndi kudulidwa amuna onse;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Koma apa pokha tidzakuvomerezani: ngati mudzakhala onga ife ndi kudulidwa amuna onse;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Tingathe kuvomera pokhapokha inu mutakhala monga momwe tiliri ifemu, ndiye kuti mutaumbala ana anu onse aamuna.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Tikuvomerani pokhapokha mutakhala ngati ife, mutachita mdulidwe ana anu onse aamuna.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 34:15
4 Mawu Ofanana  

Ili ndi pangano langa limene uzisunga pakati pa Ine ndi iwe ndi mbeu zako za pambuyo pako: azidulidwa amuna onse a mwa inu.


nati kwa iwo, Sitingathe kuchita ichi, kupereka mlongo wathu kwa mwamuna wosadulidwa; chifukwa kumeneko ndiko kutichepetsa ife.


pamenepo tidzakupatsani inu ana athu aakazi, ndipo tidzadzitengera ana anu aakazi, ndipo tidzakhala pamodzi ndi inu, ndi kukhala mtundu umodzi.


Abale, ndikupemphani, khalani monga ine, pakuti inenso ndili monga inu. Simunandichitire choipa ine;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa