Genesis 34:14 - Buku Lopatulika14 nati kwa iwo, Sitingathe kuchita ichi, kupereka mlongo wathu kwa mwamuna wosadulidwa; chifukwa kumeneko ndiko kutichepetsa ife. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 nati kwa iwo, Sitingathe kuchita ichi, kupereka mlongo wathu kwa mwamuna wosadulidwa; chifukwa kumeneko ndiko kutichepetsa ife. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Iwowo adati, “Sikungatheke kuti tilole mlongo wathu kukwatiwa ndi munthu wosaumbalidwa. Chimenechi ndi chinthu chamanyazi kwa ife. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Iwo anati, “Sitingachite zimenezo, kupereka mlongo wathu kwa munthu wosachita mdulidwe. Chimenecho ndi chinthu cha manyazi kwa ife. Onani mutuwo |