Genesis 34:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo ana ake aamuna a Yakobo anayankha Sekemu ndi Hamori atate wake monyenga, nanena, popeza anamuipitsa Dina mlongo wao, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo ana ake amuna a Yakobo anayankha Sekemu ndi Hamori atate wake monyenga, nanena, popeza anamuipitsa Dina mlongo wao, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Koma ana a Yakobe adayankha Sekemu ndi bambo wake Hamori moŵanyenga, popeza kuti Sekemu adaamchititsa manyazi Dina mlongo wao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ana a Yakobo anayankha Sekemu ndi abambo ake, Hamori mwachinyengo chifukwa mlongo wawo, Dina anali atayipitsidwa. Onani mutuwo |