Genesis 33:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo Esau anati, Zanga zikwanira; mbale wanga, khala nazo zako iwe wekha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo Esau anati, Zanga zindifikira; mbale wanga, khala nazo zako iwe wekha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Koma Esau adati, “Mbale wanga, zoŵeta zotere ndili nazo zambiri. Uli nazozi zikhale zako.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Koma Esau anati, “Mʼbale wanga, ine ndili nazo kale zambiri. Zinthu zakozi sunga.” Onani mutuwo |