Genesis 33:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo Yakobo anati, Iaitu, ngatitu ndapeza ufulu pamaso panu, mulandire mphatso yanga padzanja langa; pakuti popeza ndinaona nkhope yanu, monga anthu aona nkhope ya Mulungu, ndipo inu mwandivomereza ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo Yakobo anati, Iaitu, ngatitu ndapeza ufulu pamaso panu, mulandire mphatso yanga pa dzanja langa; pakuti popeza ndinaona nkhope yanu, monga anthu aona nkhope ya Mulungu, ndipo inu mwandivomereza ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Yakobe adati, “Ai chonde, ngati mwandikomera mtima, landirani mphatso yanga. Ine ndikamaona nkhope yanu, ndiye ngati ndaona nkhope ya Mulungu, poti mwandilandira chonchi ndi manja aŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Yakobo anati, “Chonde musatero. Ngati mwandikomera mtima, landirani mphatso yangayi kuchokera kwa ine. Pakuti ndi mmene mwandirandira bwinomu, ine ndikamaona nkhope yanu ndikuchita ngati ndikuona nkhope ya Mulungu. Onani mutuwo |