Genesis 33:11 - Buku Lopatulika11 Landiranitu mdalitso wanga umene wafika kwa inu, pakuti Mulungu wandichitira ine zaufulu, ndipo zanganso zindikwanira. Ndipo anamkakamiza, nalandira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Landiranitu mdalitso wanga umene wafika kwa inu, pakuti Mulungu wandichitira ine zaufulu, ndipo zanganso zindifikira. Ndipo anamkakamiza, nalandira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Chonde landirani mphatso ndakutengeraniyi. Mulungu adandikomera mtima, ndipo adandipatsa zosoŵa zanga zonse.” Adapitirira kumuumiriza, mpaka Esau adalandira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Chonde, landirani mphatso imene ndakutengeraniyi, popeza Mulungu wandikomera mtima kwambiri moti ndili ndi zonse zimene ndizifuna.” Ndipo popeza kuti Yakobo anamuwumiriza, Esau analandira. Onani mutuwo |