Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 33:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo adzakazi anayandikira ndi ana ao, nawerama pansi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo adzakazi anayandikira ndi ana ao, nawerama pansi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Tsono adzakazi aja adadza pamodzi ndi ana ao, nagwada pansi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Tsono antchito aja anayandikira naweramitsa mitu pansi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 33:6
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anatukula maso ake nawaona akazi ndi ana; nati, Ndani awa ali ndi iwe? Ndipo iye anati, Ndiwo ana amene Mulungu anakomera mtima kumpatsa kapolo wanu.


Ndiponso Leya ndi ana ake anayandikira nawerama pansi: pambuyo pake anayandikira Yosefe ndi Rakele, nawerama pansi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa