Genesis 33:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo Yakobo anafika ndi mtendere kumzinda wa Sekemu umene uli m'dziko la Kanani, pamene anachokera ku Padanaramu; namanga tsasa pandunji pa mzindapo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo Yakobo anafika ndi mtendere kumudzi wa Sekemu umene uli m'dziko la Kanani, pamene anachokera ku Padanaramu; namanga tsasa pandunji pa mudzipo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Pambuyo pake Yakobe adakafika bwino ku mzinda wa Sekemu m'dziko la Kanani, atabwerera kuchokera ku Mesopotamiya. Adamanga mahema pamalo pena, poyang'anana ndi mzindawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Mmene ankabwerera kuchokera ku Padanaramu, Yakobo anafika ku Salemu, mzinda wa Sekemu ku Kanaani. Anamanga msasa pamalopo moyangʼanana ndi mzindawo. Onani mutuwo |