Genesis 33:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo Yakobo anankabe ulendo wake ku Sukoti, namanga nyumba yake pamenepo, namanga makola a zoweta zake: chifukwa chake dzina lake la kumeneko ndi Sukoti. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo Yakobo anankabe ulendo wake ku Sukoti, namanga nyumba yake pamenepo, namanga makola a zoweta zake: chifukwa chake dzina lake la kumeneko ndi Sukoti. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Koma Yakobe adapita ku Sukoti, ndipo adamangako nyumba yake, pamodzi ndi makola a zoŵeta zake. Nchifukwa chake malowo adatchedwa Sukoti. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Komabe Yakobo anapita ku Sukoti. Kumeneko anamanga nyumba yake ndi makola a ziweto zake. Nʼchifukwa chake malowa amatchedwa Sukoti. Onani mutuwo |